Bible Bard
Cicē'ōẏā_BB-75_Za Mdyerekezi
- Author: Vários
- Narrator: Vários
- Publisher: Podcast
- Duration: 0:08:46
- More information
Informações:
Synopsis
Monga mabuku, Baibulo limafotokoza nkhani zambiri. Pamene tinayang'ana pa maina omwe amagwiritsira ntchito kwa Mulungu tinapeza kuti zambiri za makhalidwe a Mulungu zimawululidwa ndi maina ake (onani BB-68 Maina a Mulungu). Nkhaniyi ikufotokoza za kumene Baibulo limanena kuti mdyerekezi anachokera komanso kuti kutsutsa kwake Mulungu kunakhalako bwanji.